View Lyrics: Mwana Wanga Modal_close_icon

Viewing lyrics for Mwana Wanga by Maureen Lupo Lilanda.

Mwana wanga nvela kulila kwanga ine Chalo chili na mano Kwemuli, muzisunge Mukanitailila, ni bani bani sunge Mukani lekelela ni bani bani nyamule
Chalo chalelo chilibe malo a osapunzila Ise akale tinalibe mapunzilo apamwaba koma Lelo mwaluba ko mwachokela lelo Se ta puba, osa punzila
Mwayibabla phaala wa muteteka tinaliku ndya Mwayibala pe aabambo anu aa natisiya Umoyo watu, oo nali odonselela koma mwa luba, mwaluba
Mwana wanga nvela kulila kwanga ine Chalo chili na mano Kwemuli, muzisunge Mukanitailila, ni bani bani sunge Mukani lekelela ni bani bani nyamule
Pazaka zanga naonapo zuba na mwezi zambili Kuwama kwachalo siku sila mwana wangu Wela panyumba oopunzile Welako oo one banja lako
Zivuti zidane, no kolo wako niza nkala naa we Sininga ku tailile Sininga ku lekelele Chikondi changa chilimonga chitsime cha mandzi Chikondi changa chilimonga chitisime
Mwana wanga nvela kulila kwanga ine Chalo chili na mano Kwemuli, muzisunge Mukanitailila, ni bani bani sunge Mukani lekelela ni bani bani nyamule
Mwana wanga nvela kulila kwanga ine Chalo chili na mano Kwemuli, muzisunge Mukanitailila, ni bani bani sunge Mukani lekelela ni bani bani nyamule
Amama na nvela (child)
Kodi wanvela (mother)
Amama ni lipo (child)
Kodi ulipo (mother)
Sinizayenda (child)
Oosanisiye, oosanisiye (mother)
Amama na nvela (child)
Kodi wanvela (mother)
Amama ni lipo (child)
Kodi ulipo (mother)
Sinizayenda (child)
Oosanisiye, oosanisiye (mother)